Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili Mʼbuku la Ezara

EZARA

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Mfumu Koresi inalamula kuti kachisi amangidwenso (1-4)

    • Kukonzekera kuchoka ku ukapolo ku Babulo (5-11)

  • 2

    • Anthu amene anabwerera kuchokera ku ukapolo (1-67)

      • Atumiki a pakachisi (43-54)

      • Ana a atumiki a Solomo (55-57)

    • Zopereka zaufulu pakachisi (68-70)

  • 3

    • Anamanganso guwa nʼkuperekapo nsembe (1-6)

    • Ntchito yomanganso kachisi inayambika (7-9)

    • Anamanga maziko a kachisi (10-13)

  • 4

    • Anthu ankatsutsa ntchito yomanganso kachisi (1-6)

    • Adani analemba kalata kwa Mfumu Aritasasita (7-16)

    • Zomwe Aritasasita anayankha (17-22)

    • Ntchito yomanga kachisi inaimitsidwa (23, 24)

  • 5

    • Ayuda anayambiranso kumanga kachisi (1-5)

    • Tatenai analembera kalata Mfumu Dariyo (6-17)

  • 6

    • Dariyo anafufuza nʼkupereka lamulo (1-12)

    • Kachisi anamalizidwa nʼkutseguliridwa (13-18)

    • Anachita Pasika (19-22)

  • 7

    • Ezara anapita ku Yerusalemu (1-10)

    • Aritasasita analembera Ezara kalata (11-26)

    • Ezara anatamanda Yehova (27, 28)

  • 8

    • Anthu amene anabwerera ndi Ezara (1-14)

    • Kukonzekera ulendo (15-30)

    • Kunyamuka ku Babulo nʼkufika ku Yerusalemu (31-36)

  • 9

    • Aisiraeli anakwatira akazi a mitundu ina (1-4)

    • Pemphero la Ezara lovomereza machimo (5-15)

  • 10

    • Pangano loti achotse akazi a mitundu ina (1-14)

    • Akazi a mitundu ina anatumizidwa kwawo (15-44)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena