Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili M‘buku la Esitere

ESITERE

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Phwando la Mfumu Ahasiwero ku Susani (1-9)

    • Mfumukazi Vasiti anakana kumvera mfumu (10-12)

    • Mfumu inafunsira malangizo kwa amuna anzeru (13-20)

    • Mfumu inatumiza makalata (21, 22)

  • 2

    • Kufufuza mfumukazi yatsopano (1-14)

    • Esitere anakhala mfumukazi (15-20)

    • Moredikayi anaulula chiwembu (21-23)

  • 3

    • Hamani anakwezedwa ndi mfumu (1-4)

    • Hamani anakonza chiwembu chopha Ayuda (5-15)

  • 4

    • Moredikayi analira (1-5)

    • Moredikayi anapempha Esitere kuti athandize (6-17)

  • 5

    • Esitere anaonekera kwa mfumu (1-8)

    • Hamani anasonyeza kukwiya komanso kudzikweza (9-14)

  • 6

    • Moredikayi analemekezedwa ndi mfumu (1-14)

  • 7

    • Esitere anaulula chiwembu cha Hamani (1-6a)

    • Hamani anapachikidwa pamtengo umene anakonza (6b-10)

  • 8

    • Moredikayi anakwezedwa (1, 2)

    • Esitere anachonderera mfumu (3-6)

    • Lamulo la mfumu loti Ayuda adziteteze (7-14)

    • Ayuda anapeza mtendere ndipo anayamba kusangalala (15-17)

  • 9

    • Ayuda anapambana (1-19)

    • Anakhazikitsa chikondwerero cha Purimu (20-32)

  • 10

    • Moredikayi anakhala wamphamvu (1-3)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena