Mwana wamwamuna woyamba kubadwa aliyense ndi wa Yehova (1, 2)
Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa (3-10)
Mwana wamwamuna woyamba kubadwa aliyense ankaperekedwa kwa Mulungu (11-16)
Aisiraeli anatsogoleredwa kupita ku Nyanja Yofiira (17-20)
Chipilala cha mtambo komanso cha moto (21, 22)