Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili M‘buku la Yona

YONA

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Yona ankafuna kuthawa Yehova (1-3)

    • Yehova anayambitsa chimphepo (4-6)

    • Mavuto anayamba chifukwa cha Yona (7-13)

    • Yona anaponyedwa mʼnyanja (14-16)

    • Chinsomba chinameza Yona (17)

  • 2

    • Pemphero la Yona ali mʼmimba mwa chinsomba (1-9)

    • Chinsomba chinalavulira Yona kumtunda (10)

  • 3

    • Yona anamvera Mulungu nʼkupita ku Nineve (1-4)

    • Anthu a ku Nineve analapa atamva uthenga wa Yona (5-9)

    • Mulungu anaganiza zoti asawononge Nineve (10)

  • 4

    • Yona anakwiya ndipo ankafuna kufa (1-3)

    • Yehova anaphunzitsa Yona kukhala wachifundo (4-11)

      • “Kodi pali chifukwa choti ukwiyire choncho?” (4)

      • Anamuphunzitsa pogwiritsa ntchito chomera chamtundu wa mphonda (6-10)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena