Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili M‘buku la Zefaniya

ZEFANIYA

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Tsiku la chiweruzo la Yehova lili pafupi (1-18)

      • Tsiku la Yehova likubwera mofulumira (14)

      • Siliva ndi golide sizingapulumutse munthu (18)

  • 2

    • Funafunani Yehova tsiku la mkwiyo wake lisanafike (1-3)

      • Yesetsani kukhala olungama ndi ofatsa (3)

      • “Mwina mungadzabisike” (3)

    • Kuweruza mitundu yozungulira (4-15)

  • 3

    • Yerusalemu, mzinda wogalukira ndiponso wachinyengo (1-7)

    • Kuweruza ndiponso kubwezeretsa (8-20)

      • Kusintha nʼkuyamba kulankhula chilankhulo choyera (9)

      • Anthu odzichepetsa komanso ooneka onyozeka adzapulumutsidwa (12)

      • Yehova adzakondwera ndi Ziyoni (17)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena