Mzimu umabweretsa moyo ndi ufulu (1-11)
Mzimu umachitira umboni (12-17)
Chilengedwe chikudikira ufulu wa ana a Mulungu (18-25)
‘Mzimu umachonderera mʼmalo mwathu’ (26, 27)
Mulungu anawasankhiratu (28-30)
Tikugonjetsa zinthu zonse chifukwa cha chikondi cha Mulungu (31-39)