Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili Mʼbuku la Afilipi

AFILIPI

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Moni (1, 2)

    • Kuthokoza Mulungu; Pemphero la Paulo (3-11)

    • Uthenga wabwino unafalikira kwambiri ngakhale kuti panali mavuto (12-20)

    • Ndikhala ndi moyo kuti ndizitumikira Khristu, ndikamwalira ndipindula (21-26)

    • Makhalidwe anu azigwirizana ndi uthenga wabwino (27-30)

  • 2

    • Akhristu azikhala odzichepetsa (1-4)

    • Kudzichepetsa kwa Khristu komanso kukwezedwa kwake (5-11)

    • Yesetsani kuti mudzapulumuke (12-18)

      • Kuwala ngati zounikira (15)

    • Anatumiza Timoteyo ndi Epafurodito (19-30)

  • 3

    • Sitidalira zinthu zimene anthu amaziona kuti ndi zofunika (1-11)

      • Zinthu zonse nʼzopanda phindu chifukwa chakuti ndinadziwa Khristu (7-9)

    • Tiyesetse kuti tikalandire mphoto (12-21)

      • Nzika zakumwamba (20)

  • 4

    • Mgwirizano, kusangalala, maganizo abwino (1-9)

      • Musamade nkhawa ndi chinthu chilichonse (6, 7)

    • Anayamikira mphatso zimene Afilipi anapereka (10-20)

    • Moni womaliza (21-23)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena