AHEBERI
ZIMENE ZILI MʼBUKULI
-
Nsembe za nyama zinali zosakwanira (1-4)
Chilamulo chinkachitira chithunzi zinthu zabwino (1)
Nsembe ya Khristu ndi yothandiza mpaka kalekale (5-18)
Njira yatsopano komanso yamoyo (19-25)
Tisaleke kusonkhana pamodzi (24, 25)
Anawachenjeza zokhudza kuchimwa mwadala (26-31)
Tizikhala olimba mtima komanso achikhulupiriro kuti tipirire (32-39)