Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 4/8 tsamba 32
  • Chochitika Chofunikira Kukumbukira!—Lachiŵiri, April 10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chochitika Chofunikira Kukumbukira!—Lachiŵiri, April 10
  • Galamukani!—1990
Galamukani!—1990
g90 4/8 tsamba 32

Chochitika Chofunikira Kukumbukira!—Lachiŵiri, April 10

Panali pa Nisani 14 ya chaka cha 33 C.E. Yesu ankagaŵana chikho cha vinyo ndi mtanda wa mkate wopanda chotupitsa ndi atumwi ake. Malangizo ake? “Chitani ichi chikumbukiro changa.”—Luka 22:19. Chotero, kamodzi pachaka, Mboni za Yehova kuzungulira dziko lonse zimakumana pamodzi kukumbukira imfa ya Yesu m’njira imene iye analangizira pa usiku umene anapanga ndemanga imeneyo. Chaka chino, Nisani 14 idzayamba pa Lachiŵiri, April 10, pa kuloŵa kwa dzuŵa. Mukuitanidwa mwamanja aŵiri kudzagwirizana nafe m’msonkhano wokumbukira umenewu madzulo a Lachiŵiri limenelo. Chonde fufuzani kwa Mboni za Yehova zakumaloko kaamba ka nthaŵi yeniyeni ndi malo a kukumanako.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena