Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g03 7/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2003
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ziwawazi Zachulukiranji Chonchi?
    Galamukani!—2003
  • Chiwawa—Chifukwa Chimene Pali Kudera Nkhaŵa Komakulakula
    Galamukani!—1989
  • Chiwawa Choopsa Chikungoipiraipira Chifukwa Chiyani?
    Galamukani!—2003
  • Kodi Zachiwawa Zidzatha Padzikoli?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
Onani Zambiri
Galamukani!—2003
g03 7/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

July 8, 2003

Kodi Chiwawa Choopsa Chingadzathetsedwe?

Ana a sukulu asanu ndi atatu ataphedwa mu Ikeda ku Japan, wina amene anapulumuka analira pamaliro awo. Ziwawa zoopsa zikuchitika padziko lonse. Kodi anthu amachitiranji zinthu zoopsa chonchi? Kodi padzapezeka njira yozithetsera?

3 Chiwawa Choopsa Chikungoipiraipira Chifukwa Chiyani?

5 Kodi Ziwawazi Zachulukiranji Chonchi?

10 Kodi Njira Yeniyeni Yothetsera Vutoli Ingapezekedi?

12 Madzi Ndi Moyo

14 Lingaliro la Baibulo

Kodi Akristu Azichita Zogodomalitsa Maganizo?

19 Kodi Nkhalango Zachilengedwe za M’madera Otentha Zingatheke Kutetezedwa?

21 Kodi M’nkhalangozi Tingadulemo Mitengo Mosawononga?

26 Kodi Nkhalangozi Angaziteteze Ndani?

Kodi Ndizitani Tsoka Likandigwera? 16

Masoka adzidzidzi angapangitse ana kumadzifunsa mafunso ena ovuta kwambiri. Onani malangizo osavuta komanso olimbikitsa opezera mayankho ena ofunika kwambiri.

Mmene Ndinaphera Ludzu la Mawu a Mulungu 28

Taŵerengani za sisitere amene sankakhutira ndi za Mulungu mpaka pamene anayamba kuphunzira choonadi cha m’Baibulo chomwe chinasintha moyo wake.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

AFP PHOTO/Toshifumi Kitamura

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena