Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 8/09 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2009
  • Nkhani Yofanana
  • Tsankho Likuchitika Padziko Lonse
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi Tsankho Lidzatha Liti?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi Ndinu Wochitiridwa Tsankhu?
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kodi Tsankho Limayamba Bwanji?
    Galamukani!—2009
Onani Zambiri
Galamukani!—2009
g 8/09 tsamba 1-2

Zamkatimu

August 2009

N’chifukwa Chiyani Anthu Amasankhana?—Nanga Mungatani Ngati Ena Amakusankhani?

Tsiku lililonse anthu ambiri amasalidwa pazifukwa zosiyanasiyana. Kodi n’chiyani chimayambitsa tsankho? Ndipo kodi tsankho lidzatha?

3 N’chifukwa Chiyani Anthu Amasankhana?

4 Kodi Tsankho Limayamba Bwanji?

7 Chikondi Chimathetsa Tsankho

14 Luso Lopanga Khofi

19 Kodi N’chiyani Chinayambitsa Nkhondo ya Padziko Lonse?

22 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Abusa Ndi Apamwamba Kuposa Anthu Ena Mumpingo?

24 Makolo Ogwirizana

25 Panagona Luso!

Zigoba za Nkhono Zam’madzi

26 Kodi Mumatha Kusunga Zinthu Zanu Mwachinsinsi?

29 Kuchokera kwa Owerenga

30 Zochitika Padzikoli

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 ‘Chitseko Chimene Yehova Yekha Ndi Amene Angatsegule’

Kodi Ndingatani Ngati Mayi Kapena Bambo Anga Amwalira? 10

Imfa ya mayi kapena bambo ndi yopweteka kwambiri. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene mungachite ngati mayi kapena bambo anu amwalira?

Kumwamba Kuli Zinthu Zambiri Zodabwitsa 16

Asayansi akamaphunzira zambiri zokhudza chilengedwe, m’pamenenso amazindikira kuti zimene akudziwa n’zochepa kwambiri. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zinthu zogometsa zimene asayansi atulukira posachedwapa.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Based on NASA photo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena