Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • le tsamba 9-10
  • Mulungu Awononga Dziko Loipa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mulungu Awononga Dziko Loipa
  • Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Nkhani Yofanana
  • Chigawo 5
    Mverani Mulungu
  • Madzi Alisesa Dziko
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
  • Chingalawa cha Nowa
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Anthu 8 Anapulumuka
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Onani Zambiri
Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
le tsamba 9-10

Mulungu Awononga Dziko Loipa

18 Ana a Adamu anachuluka. Iwo anakhalanso oipa kwambiri. Mulungu anaganizira za kuwawononga.—Genesis 6:1, 5, 7

19 Koma panali munthu wabwino wotchedwa Nowa.—Genesis 6:8, 9

Yehova Mulungu anamuuza kukhoma chibwato choti iye mwini ndi banja lake akapulumukiremo pamene anthu oipa akawonongedwa. Chibwato chimenechi chinapangidwa ngati chibokosi. Chinatchedwa chingalawa.—Genesis 6:13, 14

20 Iwo analowetsa nyama zambiri m’chingalawa.—Genesis 6:19-21

21 Yehova anachititsa mvula yochuluka kwambiri kugwa. Anthu onse oipa anafa. Awo amene anali m’chingalawa anapulumuka. Kodi mukudziŵa chifukwa chake?—Genesis 6:17; 7:11, 12, 21; 1 Petro 3:10-12

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena