Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • od tsamba 213-222
  • Mlozera Nkhani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mlozera Nkhani
  • Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
od tsamba 213-222

Mlozera Nkhani

Dziwani izi: Malo amene mawu ambiri akupezeka asonyezedwa ndi mutu wa nkhani kenako ndime yake. Mwachitsanzo, mawu oyamba amene akupezeka pa mutu wakuti “Ana” ndi akuti “tchimo: 14:37.” Zimenezi zikutanthauza kuti nkhani yokhudza zoyenera kuchita ana akachita tchimo ikupezeka m’Mutu 14, ndime 37.

Akhristu omwe anasiya kulalikira: 8:26; 14:32

Akulu

abusa: 5:1-3; 14:7-12

amaikidwa ngati akwaniritsa zimene Malemba amanena: 4:8

kuchita zinthu mogwirizana: 5:21

kutetezera kuti mpingo ukhalebe woyera: 14:19-40

kuyesetsa kuti ukhale mkulu: 5:22

magulu ndi timagulu: 9:42-44

maudindo awo: 5:25-36, 40

misonkhano: 5:37

mmene tiyenera kuwaonera: 3:14; 5:38-39

okalamba kapena odwala: 5:23-24

zimene munthu angachite kuti ayenerere: 5:4-20

Alongo

kugwira ntchito yomanga: 10:21

ngati mumpingo mulibe abale oyenera kukhala pa udindo: 6:9; 7:23

sukulu zophunzitsa Baibulo: 10:17-18

Ana

akachita tchimo: 14:37

anyamata amene akufuna kukhala pa udindo: 6:14

kupita patsogolo: 8:13-15; 10:26; tsa. 179-181

kuthandiza makolo okalamba kapena amene akudwala: 12:14

misonkhano: 7:2; 11:13-14

moyo wa kusukulu: 13:22-24

Anthu osauka: 12:12-15

Apainiya: 10:11-14

Apainiya apadera: 10:11, 14, 17-18

Apainiya othandiza: 10:11-12

Atumiki othandiza

kuwayamikira: 6:1-2, 15

kuyesetsa kuti muyenerere: 6:14

ntchito zawo: 6:7-12; 11:14

zimene munthu angachite kuti ayenerere: 6:3-6

Bungwe Lolamulira

kusonyeza kuti timalikhulupirira: 3:12-15

mmene tingalidziwire: 3:1-6

n’chifukwa chiyani tiyenera kumvera bungweli: 3:9-11; 4:9-11

Chakudya Chamadzulo cha Ambuye: 7:28-30

Chikumbutso: 7:28-30

Chitsanzo chabwino

tanthauzo lake: 6:9

Gawo

kulemba zofunikira: 9:31

la kagulu ndi la munthu pa yekha: 9:31-34

la zinenero zosiyanasiyana: 9:36-37

Gulu

mbali yakumwamba: 1:8-13

“Kapolo wokhulupirika ndi wanzeru”

kumugonjera: 15:7

kusonyeza kuti timamudalira: 3:12-15

mmene tingamudziwire: 3:4-6

Komiti

ya Dziko: 5:53

ya Nthambi: 4:13; 5:51-54

ya Utumiki ya Mpingo: 5:35

Yolankhulana ndi Achipatala: 5:40

yoweruza: 14:21-28, 34-37

Yoyang’anira Nyumba ya Ufumu: 11:8

Komiti ya utumiki

(Onani Komiti ya Utumiki ya Mpingo)

Komiti ya Utumiki ya Mpingo: 5:35

Kubwezeretsa: 14:34-36

Kuchita zinthu mogwirizana

akulu: 5:13, 21

chimene chimachititsa: 1:6-7; 13:28-29

kukhalabe ogwirizana: 17:20

madalitso: 4:15; 5:57; 13:30-31

mavuto: 14:3; 17:6

motsogoleredwa ndi Khristu: 2:9-11; 4:10-11

padziko lonse: 16:6-11

Kuchotsa munthu mumpingo: 14:25-29

Kudzilekanitsa: 14:30-33

Kudzipereka ndiponso kubatizidwa

(Onani Ubatizo)

Kudzudzula: 14:4, 23-24

Kugonjera

(Onani Mutu)

Kuika chizindikiro anthu ochita zosalongosoka: 14:9-12

Kuikidwa kukhala mtumiki wa Mulungu: 8:3

Kulalikira uthenga wabwino

achinyamata: 8:13-15

gawo: 9:30-34

imayang’aniridwa ndi woyang’anira utumiki: 5:28

kuchitira lipoti: 8:19-29, 31-36

kufunika kwake: 9:5-8; 10:1-2

kugwiritsa ntchito webusaiti ya jw.org: 9:24-25

kulalikira m’magulu: 9:45-46

kulalikira mwamwayi: 9:26-29

kulimbikitsa ophunzira Baibulo kuti aziuza ena zimene akuphunzira: 8:5

kunyumba ndi nyumba: 9:3-9

kuthandiza nawo: 5:28-29, 33; 7:21; 9:7, 15, 19

kutsogolera: 5:3, 17, 29-33; 6:4

mabuku ndi magazini: 9:22-23

madera omwe anthu ake amalankhula zinenero zosiyanasiyana: 9:35-44

maonekedwe athu: 13:12

maulendo obwereza: 9:14-15

misonkhano yokonzekera utumiki wakumunda: 7:20-21

m’malo opezeka anthu ambiri: 9:11-12

m’nthawi ya atumwi: 8:1-2; 9:1, 4

ntchito yopatsidwa ndi Mulungu: 8:2

pa nthawi imene ntchito yathu ili yoletsedwa: 17:13-18

zoyenera kuchita munthu asanayambe kugwira nawo ntchitoyi: 8:6-9, 13-15

Kusamvana

kuthetsa pa nkhani zikuluzikulu: 14:13-20

kuthetsa pa nkhani zing’onozing’ono: 14:5-6

Kutumikira kumene kukufunikira ofalitsa ambiri: 10:6-9

Kuvala ndi kudzikongoletsa

amene angapatsidwe udindo: 6:9

atumiki othandiza: 6:5

kukacheza ku Beteli: 13:13

misonkhano: 11:12, 21

pochita zosangalatsa: 13:14

utumiki: 13:12

Kuvomereza kugwiritsa ntchito ndalama: 12:6, 9, 11

Lipoti la Mpingo Lolembapo Ntchito za Wofalitsa: 5:44; 8:10, 30

Mabuku

kufunika kwake mu utumiki: 9:22-23

kumene ndalama zimachokera: 12:2-4

kusamalira mabuku: 12:16

m’madera amene muli anthu a zinenero zosiyanasiyana: 9:36, 38

Mabungwe osiyanasiyana: 4:12

Madera amene anthu amalankhula zinenero zosiyanasiyana: 9:35-44

magulu ndi timagulu: 9:42-44

sukulu yophunzitsa chinenero: 10:10

tikakumana ndi munthu wolankhula chinenero china: 9:38-41

Makomiti Olankhulana ndi Achipatala ndiponso Magulu Oyendera Odwala: 5:40

Makomiti oweruza: 14:21-28, 34-37

Malipoti

kufunika kwake: 8:19-22, 31-36

ngati tachokapo kwakanthawi: 8:30

ofalitsa: 5:34; 8:10, 23-29

oyang’anira madera: 5:46, 50; 9:44

Maliro: 11:10-11

Malo a Misonkhano: 11:18-21

Maphunziro a Baibulo

kuchitira lipoti: 8:26

kulimbikitsa wophunzira kuti aziuza ena zomwe akuphunzira: 8:5

kutsogolera wophunzira ku gulu la Yehova: 9:20-21

ubwino wake: 9:16-17

Maukwati: 11:10-11

Mayesero: 13:4-5; 17:4-19

Misonkhano ya mpingo

Aisiraeli: 11:1

akulu: 5:37

ana azikhala ndi makolo awo: 11:13

cholinga: 7:1-2

kufunika kwake: 3:12; 7:4, 27; 15:7

kukambirana za malonda: 13:27

malo osonkhanako: 11:1-5, 18-19

misonkhano yachigawo: 7:25-26

misonkhano yadera: 7:24

misonkhano yokonzekera utumiki: 7:20-21; 9:45

munthawi ya atumwi: 7:3; 11:2

nkhani ya onse: 7:5-10

olandira alendo: 11:14

pa mlungu wapadera: 5:43, 47

pamene ntchito yathu ili yoletsedwa: 17:15-17

Phunziro la Baibulo la Mpingo: 7:17

Phunziro la Nsanja ya Olonda: 7:11-13

Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu: 7:14-19

yochititsidwa ndi alongo: 7:23

Misonkhano yachigawo: 7:25-27

Misonkhano yadera

(Onani Msonkhano wadera)

Mlembi: 5:27; 8:30

Mpingo

(Onaninso Nyumba ya Ufumu; Misonkhano ya mpingo)

kugwirizana: 13:28-30

umatsogoleredwa ndi Yehova: 1:3; 4:4-11

watsopano ndi waung’ono: 7:22-23

Msonkhano wadera

malo: 11:18

mmene umayendetsedwera: 5:49

ndalama zoyendetsera: 12:8-11

Mutu

m’banja: 15:9-10

m’gulu la Yehova: 1:9-10; 2:5, 9-10; 15:1-2

mumpingo: 3:14; 4:15; 15:7

olamulira akuluakulu: 15:11

Ndalama

za dera: 12:8-11

za mpingo: 11:6-7; 12:5-7

za ntchito ya padziko lonse: 11:15; 12:2-4

Ndandanda ya Msonkhano wa utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu 7:14-18

Nkhani ya onse: 7:5-10

Ntchito yopereka thandizo: 12:15; 16:11

Ntchito zomangamanga: 10:21-23

Gulu la Zomangamanga: 10:23

ongodzipereka kuchita utumiki wa zomangamanga: 10:23

othandiza pa ntchito ya zomangamanga m’dera lawo: 10:23

wochita utumiki wa zomangamanga: 10:23

wogwira ntchito ya zomangamanga m’dziko lina: 10:23

Ntchito: 13:25-26

Nyumba ya Ufumu

kuipereka: 11:4

kuisamalira: 11:7-8

kulipira zinthu zofunika: 11:6; 12:5-6

kumanga: 10:21-23; 11:4-5, 15-17

laibulale: 7:19

mipingo ingapo: 11:8-9

zochitika zapadera: 11:10-11

Ofalitsa

(Onani Ofalitsa a mpingo; Ofalitsa osabatizidwa)

Ofalitsa a mpingo

(Onaninso Ofalitsa osabatizidwa)

ana: 8:13-14

atsopano: 8:5-6

kusamuka: 8:30

kuti ayenerere kukhala ofalitsa: 8:8

kuwathandiza: 5:28-29, 33; 7:21; 9:7, 15, 19

okalamba ndi odwala: 8:29

Ofalitsa osabatizidwa

akachita tchimo: 14:38-40

ana: 8:13-15

kuti munthu ayenerere: 8:6-12

pomanga kapena kukonza Nyumba ya Ufumu: 11:17

Ofesi ya nthambi

mmene tingavalire ndi kudzikongoletsa popitako: 13:13

ngati zili zosatheka kulankhulana ndi ofesi ya nthambi: 17:15-17

ntchito zake: 4:13

zopereka zopita ku: 12:2-4

Oimira likulu: 5:55-56

Olandira alendo: 11:14

Oyang’anira

(Onani Akulu)

Phunziro la Nsanja ya Olonda: 7:11-13

Tchimo

(Onaninso Kudzilekanitsa; Kuchotsa munthu mumpingo; Kuika chizindikiro anthu ochita zosalongosoka; Kusamvana; Kubwezeretsa)

ana: 14:37

kulakwira Mkhristu mnzathu: 14:5-6, 13-20

ofalitsa osabatizidwa: 14:38-40

tchimo lalikulu: 14:21-33

zilengezo zokhudza: 14:24, 29, 33, 39-40

Timagulu ta utumiki wakumunda

kugawa ofalitsa m’timagulu: 5:35

kusamalira Nyumba ya Ufumu: 11:7

magawo: 9:31, 33

misonkhano yokonzekera utumiki wakumunda: 7:20-21

oyang’anira: 5:29-34

udindo wa atumiki othandiza: 6:12

Ubatizo

ana: tsa. 179-181

kuikidwa kukhala mtumiki wa Mulungu: 8:3

mafunso a ubatizo: tsa. 185-207

ofalitsa osabatizidwa: tsa. 182-184

pa misonkhano yadera, yachigawo: 7:24, 26

tanthauzo lake: 8:16-18

Ukhondo

makhalidwe: 13:6-7

Nyumba ya Ufumu: 11:7-8

ukhondo: 13:8-12

Umishonale: 10:15, 18

Utumiki wa pa Beteli: 10:19-20

Webusaiti ya JW.ORG: 9:24-25

Wogwirizanitsa ntchito za akulu

kuchezera kwa woyang’anira dera: 5:42-44

kuwerengera maakaunti: 12:7

Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu: 7:18

ntchito zake: 5:26

ofalitsa atsopano: 8:8, 14

ofuna kubatizidwa: 8:18; tsa. 208-212

Woyang’anira dera

amapempha zokhazikitsa mpingo: 7:22

kuchezera kwake: 5:41-48

kulankhula naye mukafuna kuwonjezera utumiki: 10:6, 10, 16, 20

kumuchereza: 5:50

magulu: 9:44

Woyang’anira utumiki: 5:28, 32; 9:31, 37, 45

Yehova Mulungu

kukhala naye pa ubwenzi: 17:1-3

Wolamulira wa Chilengedwe Chonse: 15:1-4

Yesu Khristu

kugonjera Yehova: 15:5

Mbusa Wabwino: 2:6; 5:1

Mkulu wa Ansembe: 2:4

Mpulumutsi: 2:3

Mtumiki: 8:1-2; 9:1

Mutu wa mpingo: 1:10; 2:5

Zilengezo

kubwezeretsa: 14:36

kudzilekanitsa: 14:33

kudzudzula: 14:24

ofalitsa osabatizidwa: 8:12; 14:39-40

za wochotsedwa: 14:29

zopereka: 12:6

Zochitika za kusukulu: 13:22-24

Zolinga

kuphunzira chinenero china: 10:10

kutumikira kumene kukufunika ofalitsa ambiri: 10:6-9

kutumikira pa Beteli: 10:19-20

kuyang’anira dera: 10:16

ntchito yomanga: 10:21-23

ofalitsa: 10:4-5

sukulu zophunzitsa Baibulo: 10:17-18

ubwino wokhala nazo: 10:24-26

umishonale: 10:15

upainiya: 10:11-14

zotheka kuzikwaniritsa: 8:37

Zopereka: 3:13; 11:6-7, 15; 12:2-11

Zosangalatsa: 13:15-21

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena