Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 4
  • “Yehova Ndi M’busa Wanga”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Yehova Ndi M’busa Wanga”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Yehova Ndi M’busa Wanga”
    Imbirani Yehova
  • “Yehova ndi Mbusa Wanga”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 4

NYIMBO 4

“Yehova Ndi M’busa Wanga”

Losindikizidwa

(Salimo 23)

  1. 1. Yehova ndi M’busa wanga

    Sindidzasowa kanthu.

    Amadziwa zofuna zanga

    Zomwe ndi zofunika.

    Amanditsogolelanso

    M’malo otetezeka.

    Mwachikondi chakedi chosatha

    Wandipatsa mtendere.

    Mwachikondi chake chosatha

    Wandipatsa mtendere.

  2. 2. Zochita zanu n’zabwino,

    Zonse n’zachilungamo.

    Zochita zanga nthawi zonse

    Zikulemekezeni.

    Pamene ndikuvutika

    Mumandithandizadi.

    Sindidzaopatu chilichonse

    Chifukwa muli nane.

    Sindidzaopa chilichonse

    Chifukwa muli nane.

  3. 3. M’lungu ndinu M’busa wanga,

    Ndidzakutsatirani.

    Mumandilimbikitsa ndithu.

    Mumandipatsa zonse.

    Poti ndinudi wamphamvu

    Ndimakudalirani.

    Kukoma mtima kwanu kosatha

    Muzindisonyezabe.

    Kukoma mtimatu kosatha

    Muzindisonyezabe.

(Onaninso Sal. 28:9; 80:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena