Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 21
  • Muziika Ufumu Pamalo Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muziika Ufumu Pamalo Oyamba
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova
  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 21

NYIMBO 21

Muziika Ufumu Pamalo Oyamba

Losindikizidwa

(Mateyu 6:33)

  1. 1. Chinthu chapadera chomwe

    Tikuchidikirira

    Ndi Ufumu wa Mulungu

    Womwe ukonze zonse.

    (KOLASI)

    Muike Ufumu wake

    Poyamba nthawi zonse

    Ndipo muzimutamanda

    Ndi kumutumikira.

  2. 2. Musade nkhawa za mawa,

    Za chakudya ndi madzi.

    Mulungu adzatipatsa

    Zofunikira zonse.

    (KOLASI)

    Muike Ufumu wake

    Poyamba nthawi zonse

    Ndipo muzimutamanda

    Ndi kumutumikira.

  3. 3. Choncho muzilalikira.

    Muzithandiza anthu

    Kuti adalire M’lungu

    Ndi Ufumu wakenso.

    (KOLASI)

    Muike Ufumu wake

    Poyamba nthawi zonse

    Ndipo muzimutamanda

    Ndi kumutumikira.

(Onaninso Sal. 27:14; Mat. 6:34; 10:​11, 13; 1 Pet. 1:21.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena