Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 23
  • Yehova Wayamba Kulamulira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Wayamba Kulamulira
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Iri Nditsiku la Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Muziika Ufumu Pamalo Oyamba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 23

NYIMBO 23

Yehova Wayamba Kulamulira

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 11:15)

  1. 1. Ufumu wa Mulungu

    ukulamuliradi.

    Khristu ndiye mwala mu Ziyoni.

    Tonse tikweze mawu,

    tiimbire Mulungu.

    Yesu wakhala pa

    Mpando wachifumu.

    (KOLASI)

    Ufumu ubweretsa chani?

    Chilungamo, choonadi.

    Udzabweretsanso chiyani?

    Moyo wosatha padziko.

    Tamandani Yesu Mfumu,

    Iye ndi wachikondi.

  2. 2. Khristu ali pampando.

    Amagedo ifika

    Kudzawononga anthu oipa.

    Choncho tilalikire

    kuti ambiri amve

    Ndipo ofatsa abwere

    kwa Mulungu.

    (KOLASI)

    Ufumu ubweretsa chani?

    Chilungamo, choonadi.

    Udzabweretsanso chiyani?

    Moyo wosatha padziko.

    Tamandani Yesu Mfumu,

    Iye ndi wachikondi.

  3. 3. Tilemekeze Mfumu

    yomwe ndi yachikondi.

    Yatumidwa ndi Yehova M’lungu.

    Tizipempha Yehova

    kuti atithandize,

    Chifukwa oipa

    adzawonongedwa.

    (KOLASI)

    Ufumu ubweretsa chani?

    Chilungamo, choonadi.

    Udzabweretsanso chiyani?

    Moyo wosatha padziko.

    Tamandani Yesu Mfumu,

    Iye ndi wachikondi.

(Onaninso 2 Sam. 7:​22; Dan. 2:​44; Chiv. 7:​15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena