Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w87 2/1 tsamba 13
  • Wamitala Ndiponso Mmapondera Apeza Chowonadi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Wamitala Ndiponso Mmapondera Apeza Chowonadi
  • Nsanja ya Olonda—1987
  • Nkhani Yofanana
  • Isake Apeza Mkazi Wabwino
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • Abulahamu Anasonyeza Kuti Anali Wokhulupirika
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Nsanja ya Olonda—1987
w87 2/1 tsamba 13

Wamitala Ndiponso Mmapondera Apeza Chowonadi

Mwamuna wa ku Afirika wotchedwa Isake, limodzi ndi amuna ena, anachoka ku Tchalitchi cha Apositoliki cha mmudzi mwake chifukwa sichinali kuchita zomwe chinaphunzitsa. Pambuyo pake onse, kuphatikizapo akazi awo, anakhala Mboni za Yehova​—kupatulapo Isake. Iwo analingalira za kumuchezera ndi kumuwuza kuti apeza chowonadi. Isake, panthawiyo, anali mapondera wopambana ndipo anali ndi akazi ambiri. Pambuyo pa kuphunzira kabukhu ka Sangalalani ndi Moyo Pa Dziko Lapansi Kosatha! lochita ndi njira yake ya moyo, Isake anasiya umapondera wake, womwe umamubweretsera ndalama zambiri, ndipo akazi ake kusiyapo mkazi wamkulu. lye analembetsa ukwati wake kwa mkazi wake wamkulu, yemwe anali ndi zaka 63 (iye anali 68). lye akuti akumva kukhala “wachimwemwe kwambiri ndi womasuka sawopanso mizimu.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena