Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w94 3/1 tsamba 32
  • “Tiyeni Tiyambe Taŵerenga Kwambiri Tisananyozere”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Tiyeni Tiyambe Taŵerenga Kwambiri Tisananyozere”
  • Nsanja ya Olonda—1994
Nsanja ya Olonda—1994
w94 3/1 tsamba 32

“Tiyeni Tiyambe Taŵerenga Kwambiri Tisananyozere”

IZO nzimene munthu wina wa ku New Zealand ananena ponena za Nsanja ya Olonda, magazini amene mukuŵerenga. Ponena za nkhani yonena za galeta lakumwamba la Mulungu lofotokozedwa mu Ezekieli chaputala 1, munthuyo analemba kuti:

“Chilichonse cha zamoyo zinayi zimenezi, kapena akerubi, chinali ndi mapiko anayi ndi nkhope zinayi. Zinali ndi nkhope ya mkango, yoimira chilungamo cha Yehova; nkhope ya ng’ombe, yoimira mphamvu ya Mulungu; nkhope ya chiwombankhanga, yotanthauza nzeru zake; ndi nkhope ya munthu, yosonyeza chikondi cha Yehova.

“Nditaŵerenga zimenezi mobwerezabwereza, mtima wanga unakhudzidwa kwambiri. Misozi inadzala m’maso mwanga, ija yachimwemwe. Malingaliro omwe ndinakhala nawo panthaŵi yomweyo anali akuti, ‘Muyenera kukhala wokongola ndi wabwino chotani nanga, Yehova!’ Malingaliro atsopano ameneŵa kulinga kwa Yehova Mulungu ameneyu amene ndatonza kwazaka zambiri akundidabwitsa, pokhala munthu wakudziko mmene ndilirimu. Ndikuti ‘zikomo’ kwa Mboni za Yehova, ndipo kwa ambiri onga ine, ndikuti, ‘Tiyeni tiyambe taŵerenga kwambiri tisananyozere.’”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena