Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w98 4/1 tsamba 32
  • Dzakhale Nafeni Pachochitika Chapadera Loŵeruka, April 11, 1998

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dzakhale Nafeni Pachochitika Chapadera Loŵeruka, April 11, 1998
  • Nsanja ya Olonda—1998
Nsanja ya Olonda—1998
w98 4/1 tsamba 32

Dzakhale Nafeni Pachochitika Chapadera Loŵeruka, April 11, 1998

MBONI ZA YEHOVA zikukupemphani kuti mudzakhale nazo pokumbukira mphatso ya Mulungu ya Mwana wake, Yesu Kristu. Mphatso imeneyi inapatsa anthu chiyembekezo cha kukhala ndi moyo wosatha padziko lapansi.​—Yohane 3:16.

Chaka chino Chikumbutso cha imfa ya Yesu chidzakhalapo Loŵeruka, April 11, dzuŵa litaloŵa. Tsiku limenelo likulingana ndi tsiku la Nisani 14 la pakalenda ya m’Baibulo yotsatira kayendedwe ka mwezi. Chonde funsani Mboni za Yehova za kwanuko kuti zikuuzeni malo ndi nthaŵi yake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena