Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 January tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 January tsamba 1-2

Zamkatimu

January 2016

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse​—ku Oceania

MLUNGU WA FEBRUARY 29, 2016–MARCH 6, 2016

7 “Mupitirize Kukonda Abale”

Kodi lemba la chaka cha 2016 ndi liti? Kodi tiyenera kuganizira chiyani tikamaona lembali m’Nyumba ya Ufumu? Nkhaniyi ikuyankha mafunso amenewa.

MLUNGU WA MARCH 7-13, 2016

12 Tiziyamikira ‘Mphatso Yaulere’ Imene Mulungu Anatipatsa

Mtumwi Paulo ananena kuti Yehova anatipatsa ‘mphatso yaulere, imene sitingathe n’komwe kuifotokoza.’ (2 Akor. 9:15) Kodi mphatsoyi ndi chiyani? Kodi imatithandiza bwanji kutsanzira Yesu Khristu, kukonda abale athu ndiponso kukhululukira ena ndi mtima wonse? Nkhaniyi ikuyankha mafunsowa komanso ikufotokoza zinthu zina zimene tingachite pa nthawi ya Chikumbutso.

MLUNGU WA MARCH 14-20, 2016

17 Mzimu Umachitira Umboni Limodzi ndi Mzimu Wathu

MLUNGU WA MARCH 21-27, 2016

22 “Tipita Nanu Limodzi”

Nkhani ziwirizi zikufotokoza mmene munthu amadziwira kuti wadzozedwa komanso zimene zimachitika akadzozedwa. Koma kodi odzozedwa ayenera kudziona bwanji? Nanga tiyenera kudandaula ngati chiwerengero cha anthu amene anadya zizindikiro pa Chikumbutso chakwera? Nkhanizi zikuyankhanso mafunso amenewa.

MLUNGU WA MARCH 28, 2016–APRIL 3, 2016

28 Timasangalala Kwambiri Kugwira Ntchito Limodzi ndi Mulungu

Kuyambira kale, Yehova wakhala akulola atumiki ake kuti azigwira naye ntchito pokwaniritsa cholinga chake. Iye akufuna kuti uthenga wabwino ulalikidwe padziko lonse ndipo watipempha kuti tizigwira naye ntchitoyi. Nkhaniyi ikufotokoza madalitso amene timapeza chifukwa chogwira ntchito limodzi ndi Mulungu.

CHITHUNZI CHA PACHIKUTO:

MADAGASCAR

Mpainiya akulalikira munthu wina amene akuyendetsa ngolo mumsewu umene uli ndi mitengo ya malambe, mumzinda wa Morondava ku Madagascar

KULI OFALITSA

29,963

MAPHUNZIRO A BAIBULO

77,984

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO

135,122

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena