Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 February tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 February tsamba 1-2

Zamkatimu

February 2016

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

3 Mbiri ya Moyo Wanga​—Yehova Wandithandiza Kwambiri Pomutumikira

MLUNGU WA APRIL 4-10, 2016

8 Abulahamu Anali “Bwenzi” la Yehova

MLUNGU WA APRIL 11-17, 2016

13 Tsanzirani Anthu Amene Anali pa Ubwenzi Wolimba ndi Yehova

Nkhanizi zitithandiza kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova. M’nkhani yoyamba tikambirana za chitsanzo cha Abulahamu. M’nkhani yachiwiri tikambirana za Rute, Hezekiya ndiponso Mariya, mayi ake a Yesu.

18 Kodi Mungatani Kuti Muzitumikirabe Yehova Mosangalala?

MLUNGU WA APRIL 18-24, 2016

21 Muzikhala Okhulupirika kwa Yehova

MLUNGU WA APRIL 25, 2016–MAY 1, 2016

26 Tizitsanzira Atumiki a Yehova Amene Anali Okhulupirika

M’nkhanizi tikambirana chitsanzo cha Mfumu Davide komanso cha anthu amene anakhalapo pa nthawi yake. Nkhani zimenezi zitithandiza kuona mmene mfundo za m’Baibulo zingatithandizire kukhala okhulupirika kwa Yehova pa zinthu zosiyanasiyana.

31 Kale Lathu

CHITHUNZI CHA PACHIKUTO:

BENIN

M’mudzi wa Hétin, anthu ambiri amamanga nyumba zawo paphaka ndipo amagwiritsa ntchito mabwato akafuna kupita kwinakwake. M’mudziwu muli mipingo itatu, ofalitsa 215 komanso apainiya 28. N’zosangalatsa kuti mu 2014, anthu okwana 1,600 anapezeka pa Chikumbutso

KULI ANTHU

10,703,000

KULI OFALITSA

12,167

KULI APAINIYA OKHAZIKIKA

1,492

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena