Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 March tsamba 2
  • Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 March tsamba 2

Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA MAY 2-8, 2016

3 Achinyamata, Kodi Ndinu Okonzeka Kubatizidwa?

MLUNGU WA MAY 9-15, 2016

8 Achinyamata, Kodi Mungakonzekere Bwanji Kubatizidwa?

Timasangalala kwambiri kuona kuti chaka chilichonse anthu pafupifupi 250,000 amabatizidwa. Ambiri mwa anthuwa amakhala achinyamata ndipo ena amakhala asanakwanitse zaka 13. Kodi amadziwa bwanji kuti ndi okonzeka kudzipereka kwa Yehova? Nanga amakonzekera bwanji kuti ayenerere kubatizidwa? Nkhani ziwirizi zikuyankha mafunso amenewa.

MLUNGU WA MAY 16-22, 2016

13 Kodi Tingathandize Bwanji Kulimbitsa Mgwirizano Wathu?

Tikamayesetsa kuchita zinthu mogwirizana, Yehova amatidalitsa. Nkhaniyi ili ndi malangizo amene angatithandize kuti tizigwirizana mumpingo, m’banja komanso pogwira ntchito yolalikira.

MLUNGU WA MAY 23-29, 2016

18 Yehova Amatsogolera Anthu Ake Kuti Adzapeze Moyo

Yehova wakhala akutsogolera bwino anthu ake. Nkhaniyi ikufotokoza kuti iye amasintha malangizo amene amapereka kwa anthu ake kuti agwirizane ndi mmene zinthu zilili pa nthawiyo. Ikufotokozanso zimene tiyenera kuchita posonyeza kuti timafuna kuti Yehova azititsogolerera.

23 Kodi Mungathandize Bwanji Mpingo Wanu?

26 Muzitsanzira Aneneri

29 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena