Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w17 February tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17 February tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA APRIL 3-9, 2017

3 Cholinga cha Yehova Chidzakwaniritsidwa

MLUNGU WA APRIL 10-16, 2017

8 Dipo Ndi ‘Mphatso Yangwiro’ Yochokera kwa Atate

Dipo la Khristu ndi lofunika kwambiri pa chikhulupiriro chathu. Limathandizanso kwambiri kuti cholinga cha Mulungu chokhudza anthu chidzakwaniritsidwe. Nkhani ziwirizi zikufotokoza chifukwa chake panafunika dipo, zimene linakwaniritsa komanso zimene tingachite posonyeza kuti timayamikira mphatso yamtengo wapatali imeneyi.

13 Mbiri ya Moyo Wanga​—Mulungu Anatisonyeza Kukoma Mtima Kwakukulu M’njira Zambiri

MLUNGU WA APRIL 17-23, 2017

18 Yehova Amatsogolera Anthu Ake

MLUNGU WA APRIL 24-30, 2017

23 Kodi Ndi Ndani Akutsogolera Anthu a Mulungu Masiku Ano?

Yehova wakhala akusankha anthu kuti azitsogolera anthu ake. Kodi tikudziwa bwanji kuti Yehova amathandiza anthu amenewa komanso kapolo wokhulupirika masiku ano? Nkhani ziwirizi zikufotokoza zinthu zitatu zomwe zimatithandiza kudziwa anthu amene Mulungu akuwagwiritsa ntchito.

29 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

31 Kale Lathu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena