Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w17 September tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17 September tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA OCTOBER 23-29, 2017

3 Tiziyesetsa Kukhala Odziletsa

Yehova ndi chitsanzo chabwino kwambiri pa nkhani yodziletsa. Kodi tingamutsanzire bwanji posonyeza khalidwe limeneli? Nanga n’chiyani chingatithandize kukhala odziletsa?

MLUNGU WA OCTOBER 30, 2017–NOVEMBER 5, 2017

8 Tizitsanzira Yehova pa Nkhani ya Chifundo

Kodi munthu angasonyeze bwanji chifundo? Yehova ndiponso Yesu ndi zitsanzo zabwino kwambiri pa nkhaniyi. Koma kodi tingawatsanzire bwanji? Nanga kuchita zimenezi kungatithandize bwanji ifeyo?

13 Mbiri ya Moyo Wanga​—Ndakhala ndi Mwayi Wotumikira Limodzi ndi Abale Okhulupirika

MLUNGU WA NOVEMBER 6-12, 2017

18 “Mawu a Mulungu Wathu Adzakhala Mpaka Kalekale”

MLUNGU WA NOVEMBER 13-19, 2017

23 ‘Mawu a Mulungu Ndi Amphamvu’

N’zolimbikitsa kwambiri kuti masiku ano Baibulo limapezeka m’zilankhulo zambiri. Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikira kuti Baibulo limapezeka m’chilankhulo chimene timachidziwa bwino? Nkhani ziwirizi zitithandiza kuyamikira kwambiri Baibulo komanso kukonda kwambiri Mulungu yemwe anatipatsa Baibulolo.

MLUNGU WA NOVEMBER 20-26, 2017

28 ‘Limba Mtima Ndipo Ugwire Ntchitoyi’

Akhristu amafunika kukhala olimba mtima. Kodi zitsanzo za anthu amene analimba mtima zingatithandize bwanji? Kodi achinyamata, makolo, alongo achikulire komanso abale obatizidwa angasonyeze bwanji kuti ndi olimba mtima komanso ofunitsitsa kugwira ntchito zabwino?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena