Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 December tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 December tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA FEBRUARY 4-10, 2019

3 “Tidzaonana M’Paradaiso”

Akhristu oona amayembekezera kwambiri kudzakhala m’paradaiso. Nkhaniyi ikufotokoza mfundo za m’Malemba zotithandiza kuyembekezera zimenezi komanso tanthauzo la lonjezo la Yesu lokhudza paradaiso.

8 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

9 Kodi Mukukumbukira?

MLUNGU WA FEBRUARY 11-17, 2019

10 Tizilemekeza “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”

Nkhaniyi ikufotokoza zimene Baibulo limanena pa nkhani ya kulemekeza ukwati. Kodi tingasonyeze bwanji kuti timalemekeza ukwati? Nanga tingatsatire bwanji zimene Baibulo limanena pa nkhani ya kuthetsa banja komanso kupatukana?

15 Mbiri ya Moyo Wanga​—‘Yehova Watichitira Zinthu Zabwino’

MLUNGU WA FEBRUARY 18-24, 2019

19 Achinyamata, Mlengi Wanu Amafuna Kuti Muzikhala Osangalala

MLUNGU WA FEBRUARY 25, 2019–MARCH 3, 2019

24 Achinyamata, Mukhoza Kukhala ndi Moyo Wosangalala

Nthawi zambiri achinyamata amafunika kusankha zochita pa nkhani zikuluzikulu monga zimene angachite pa moyo wawo. Aphunzitsi komanso akuluakulu ena m’dzikoli amalimbikitsa anthu kuti azifunafuna maphunziro apamwamba komanso ntchito yabwino. Koma Yehova amalimbikitsa achinyamata kuti aziika kumutumikira pamalo oyamba. Nkhani ziwirizi zikusonyeza kuti ndi nzeru kumvera Mulungu.

29 “Wolungama Adzakondwera mwa Yehova”

32 Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! a 2018

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena