Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/95 tsamba 2
  • Konzekerani Chikumbutso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Konzekerani Chikumbutso
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1995
  • Nkhani Yofanana
  • Zikumbutso za Chikumbutso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1996
  • Zikumbutso za pa Chikumbutso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
  • Zofunika Kukumbukira Panthaŵi ya Chikumbutso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2001
  • Zokumbutsa za Chikumbutso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—1995
km 4/95 tsamba 2

Konzekerani Chikumbutso

Kodi aliyense, kuphatikizapo mlankhuli, wadziŵitsidwa za nthaŵi yeniyeni ndi malo a chochitikacho? Kodi mlankhuli akudziŵa kuti programuyo siyenera kuposa mphindi 45?

Kodi pali amene wasankhidwa kupeza zizindikiro zake? (Onani Nsanja ya Olonda ya February 15, 1990, masamba 16-18.) Kodi makonzedwe a kulinganiza thebulo loyalidwapo nsalu yaudongo ndi matambula ndi mbale zake zokwanira apangidwa?

Kodi makonzedwe a kuyeretsa Nyumba Yaufumu pasadakhale ndi pambuyo pake apangidwa? Kodi akalinde ndi oyendetsa zizindikiro asankhidwa? Kodi msonkhano wa kuonana nawo kuti afotokozeredwe ntchito zawo wachitidwa? Kodi ndi njira zotani zimene zidzatsatiridwa kuti mutsimikizire kuti zizindikirozo zafika kwa onse mokwanira?

Kodi makonzedwe a kuthandiza abale ndi alongo okalamba ndi odwala kufikapo apangidwa? Ngati pali aliyense wa odzozedwa amene angakhale wobindikiritsidwa ndi wosakhoza kupezekapo, kodi makonzedwe a kumperekera zizindikiro apangidwa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena