Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/96 tsamba 7
  • Bokosi la Mafunso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bokosi la Mafunso
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1996
Utumiki Wathu wa Ufumu—1996
km 7/96 tsamba 7

Bokosi la Mafunso

◼ Kodi ndi misonkhano iti ya mpingo imene iyenera kuchitidwa mkati mwa mlungu wa msonkhano wadera?

Msonkhano wokha umene mipingo iyenera kuuchita m’mlungu wa msonkhano wadera ndiwo Phunziro la Buku la Mpingo. Misonkhano ina inayi imaloŵedwa m’malo m’njira ina ndi programu ya msonkhano wadera. Makonzedwe ameneŵa adzathandiza aliyense wa ife kukonzekerera ndi kulinganiza zinthu pasadakhale kaamba ka programu ya kudyetsedwa imene yakonzedwa kaamba ka ife ndi kapolo wokhulupirika ndi wanzeru.—Mat. 24:45-47; Sal. 122:1; 93:5.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena