Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/02 tsamba 2
  • ‘Muzipatulapo Kanthu’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Muzipatulapo Kanthu’
  • Utumiki wathu wa Ufumu—2002
  • Nkhani Yofanana
  • Aliyense Angapatse Yehova Chinachake
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2008
  • Anthu Opatsa Amakhala Osangalala
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • ‘Muziika Kenakake Pambali’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Kodi Mukukumbukira?
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Utumiki wathu wa Ufumu—2002
km 1/02 tsamba 2

‘Muzipatulapo Kanthu’

Mu mpingo woyambirira wachikristu, anali ndi zosoŵa zakuthupi zofunika kuzisamalira. Malinga ndi mmene munthu aliyense anali kupezera, analimbikitsidwa kuti ‘azipatulapo kanthu’ kukhala chopereka kuti asamalire zosoŵazo. (1 Akor. 16:1-3, Chipangano Chatsopano Cholembedwa m’Chicheŵa Chamakono) Chifukwa cha kuolowa manja kwawo, onse anasangalala kupereka kwa “Mulungu mwa mayamiko ambiri.”—2 Akor. 9:11, 12.

Lerolino ntchito ya padziko lonse ya anthu a Yehova ikukulirakulira, ndipo ikufuna ndalama zambiri. Ndiye chifukwa chake ifenso tiyenera ‘kupatulapo kanthu’ nthaŵi zonse kuti tithandize pa kusoŵako. (2 Akor. 8:3, 4) Tingapereke chuma m’njira zambiri. (Onani Nsanja ya Olonda ya November 1, 2001, masamba 28-9.) Timaona zimenezi monga mwayi umene umadzetsa chimwemwe chenicheni ndipo m’pake kutero.—Mac. 20:35.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena