Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/03 tsamba 7
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
km 7/03 tsamba 7

Zilengezo

◼ Mabuku ogaŵira mu July ndi August: Gwiritsani ntchito bulosha la Njira ya ku Moyo Wosatha—Kodi Mwaipeza? Mabulosha ameneŵa akatha, mungagwiritse ntchito bulosha lina lililonse. Khalani ndi cholinga choyambitsa maphunziro a Baibulo mukapeza munthu wachidwi. September: Chinsinsi cha Chimwemwe cha Banja kapena Munthu Wamkulu Woposa Onse Amene Anakhalako. October: Gaŵirani magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! Ngati mwapeza munthu wachidwi, gaŵirani bulosha la Mulungu Amafunanji, ndipo yesetsani kuyambitsa maphunziro a Baibulo.

◼ Kuyambira mu September, oyang’anira madera adzakamba nkhani ya onse ya mutu wakuti “N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuopa Mulungu Woona?”

◼ Misonkhano Yachigawo: Tasintha masiku a Misonkhano Yachigawo ku Thete ndi ku Ntcheu. Misonkhano iŵiri imeneyi idzachitika pa September 5 mpaka 7, 2003 m’malo mwa pa August 8 mpaka 10, 2003 ku Thete ndi pa August 15 mpaka 17, 2003 ku Ntcheu.

◼ Zofalitsa Zatsopano Zimene Zilipo:

Imbirani Yehova Zitamando—Zilembo Zazikulum’Chichewa. (Imeneyi ndi nyimbo yokhala ndi zilembo zazikulu koma yopanda madododo, yoyenera anthu amene saona bwino.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena