Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/09 tsamba 4
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 12/09 tsamba 4

Zilengezo

◼ Mabuku ogawira mu December: Munthu Wamkulu Woposa Onse Amene Anakhalako. January 2010: Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? February: Chinsinsi cha Chimwemwe cha Banja. Ndipo mu March: Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?

◼ Chikumbutso cha chaka cha 2011 chidzachitika Lamlungu, pa April 17, dzuwa litalowa. Taneneratu zimenezi kuti abale apezeretu malo ena ngati mipingo ingapo imagwiritsa ntchito Nyumba ya Ufumu imodzi.

◼ Posachedwapa titumizira mpingo uliwonse timapepala toitanira anthu ku Chikumbutso ta m’chinenero chimene mpingowo umagwiritsa ntchito. Ngati m’gawo lanu muli anthu a zinenero zina ndipo mukufuna kuti tikutumizireni timapepala ta zinenero zimenezo, muyenera kuitanitsa timapepalato mwamsanga pa Fomu Yofunsira Mabuku (S-14) kapena pa adiresi ya pa Intaneti ya jw.org. Timapepalati tidzakhalapo m’Chichewa, m’Chingelezi ndi m’Chitumbuka.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena