Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/11 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 5/11 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Magazini athu amakhala ndi uthenga wopulumutsa moyo. Choncho n’zolimbikitsa kuona kuti anthu ambiri akuwerenga magaziniwa. Mwachitsanzo, m’mwezi wa December 2010, tinagawira anthu magazini okwanira 408,865. Komanso tinachititsa maphunziro a Baibulo 82,720. Izi zikutanthauza kuti wofalitsa aliyense anali ndi phunziro la Baibulo. Mwezi umenewu ndi umene tinachititsa maphunziro a Baibulo ambiri kuposa mwezi wina uliwonse m’chaka chonsecho. Tikukhulupirira kuti ambiri mwa anthu amenewa apindula ndi madzi a moyo amene akuwalandirawa. (Chiv. 22:17) Komanso tinasangalala titalandira malipoti ambiri a miyezi yam’mbuyo. Tikukhulupirira kuti mabungwe a akulu apitiriza kuonetsetsa kuti akutumiza malipoti autumiki wakumunda ku ofesi ya nthambi mwezi uliwonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena