Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/11 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 11/11 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Lemba la Yesaya 60:22 limati: “Wamng’ono adzasanduka anthu 1,000, ndipo wochepa adzasanduka mtundu wamphamvu. Ineyo Yehova ndidzafulumizitsa zimenezi pa nthawi yake.” Monga mbali ya kukwaniritsidwa kwa ulosi umenewu, m’chaka cha utumiki chapitachi, m’Malawi muno munapangidwa mipingo yatsopano yokwana 49. Umenewutu ndi umboni wakuti Yehova akudalitsa ntchito yake m’gawo la nthambi yathu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena