Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/12 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 6/12 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’mwezi wa January chaka chino tinathera maola okwana 1,219,526 mu utumiki wakumunda. Komatu m’mwezi umenewu chakudya chimakhala chovuta kupeza m’Malawi muno. Komanso, abale athu ambiri ali m’mavuto azachuma. Choncho, tikukuyamikirani kwambiri chifukwa chopitiriza kulalikira ndiponso kuphunzitsa anthu choonadi ngakhale mukukumana ndi mavuto ambiri m’masiku otsiriza ano.—Mat. 6:33.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena