Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/12 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 8/12 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Yehova akudalitsa ntchito yathu m’Malawi muno. Tikutero chifukwa m’chaka chautumiki cha 2012, mipingo 29 yatsopano inakhazikitsidwa m’dziko lathuli. Sitikukayikira kuti Mulungu wathu wabwino Yehova, apitiriza kudalitsa anthu ake ndi zinthu zambiri zabwino m’chaka chautumiki cha 2013 chimene chiyambe mu September. Tikukuthokozani abale ndi alongo nonse chifukwa choika zinthu zauzimu patsogolo m’moyo wanu.—Mal. 3:10; Mat. 6:33.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena