Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/13 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 10/13 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’Malawi muno muli mipingo 1,349 ndipo ofalitsa alipo 88,052. Pa mipingo imeneyi, mipingo 1,241 ndi ya Chichewa, 96 ya Chitumbuka, 47 ya Chitonga, 6 ya Chingelezi ndipo 5 ndi ya Chinenero Chamanja. Komanso pali magulu a Chinenero Chamanja m’malo ngati Nkhata Bay, Kasungu, Lilongwe Rural, Mchinji, Balaka, Mangochi, Zomba, Mulanje Boma, Migowi, Nchalo komanso m’madera ena. Tilinso ndi dera limodzi la Chinenero Chamanja, madera atatu a Chitonga, 5 a Chitumbuka ndiponso 53 a Chichewa. Madera onse alipo 62. Tikukhulupirira kuti Yehova apitiriza kudalitsa khama lathu pamene tikuyesetsa kulalikira uthenga wabwino m’madera onse a m’dziko muno.—Aroma 12:11.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena