Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 July tsamba 7
  • July 25-31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 25-31
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 July tsamba 7

July 25-31

MASALIMO 79-86

  • Nyimbo Na. 138 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Munthu Wofunika Kwambiri pa Moyo Wanu ndi Ndani?”: (10 min.)

    • Sal. 83:1-5​—Cholinga chathu chachikulu chizikhala kulemekeza dzina la Yehova komanso ulamuliro wake (w08 10/15 13 ndime 7-8)

    • Sal. 83:16​—Tikamakhalabe okhulupirika ngakhale pamavuto, dzina la Yehova limalemekezedwa (w08 10/15 15 ndime 16)

    • Sal. 83:17, 18​—Yehova ndi wofunika kwambiri m’chilengedwe chonse (w11 5/15 16 ndime 1-2; w08 10/15 15-16 ndime 17-18)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Sal. 79:9​—Kodi lemba limeneli lingatithandize bwanji kudziwa zimene tinganene m’mapemphero athu? (w06 7/15 12 ndime 5)

    • Sal. 86:5​—Kodi Yehova ndi “wokonzeka kukhululuka” motani? (w06 7/15 12 ndime 9)

    • Kodi ndaphunzira chiyani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Sal. 85:8–86:17

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) fg mutu 7 ndime 1

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) fg mutu 7 ndime 3

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg mutu 7 ndime 7-8

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 111

  • Kodi Mulungu Ali Ndi Dzina?: (15 min.) Yambani ndi kuonera vidiyo yakuti Kodi Mulungu Ali Ndi Dzina? (Kuti mupeze vidiyoyi, pitani pamene palembedwa kuti, MABUKU > MAVIDIYO. Kenako pitani pomwe pali kabuku ka Uthenga Wabwino. Vidiyoyi ikupezeka paphunziro 2 lakuti “Kodi Mulungu Ndani?”) Kenako kambiranani mafunso otsatirawa: Kodi tingagwiritse ntchito bwanji vidiyoyi tikamalalikira mwamwayi, pamalo opezeka anthu ambiri komanso tikamalalikira kunyumba ndi nyumba? Kodi ndi zosangalatsa zotani zimene zinakuchitikirani pamene munkagwiritsa ntchito vidiyoyi?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 3 ndime 1-13, bokosi patsamba 29

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 143 ndi Pemphero

    Kumbukirani kuti, muyenera kuika nyimboyi kuti onse amvetsere, kenako muibwerezenso kuti onse aimbe nawo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena