Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsamba 4
  • September 12-18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 12-18
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 September tsamba 4

September 12-18

Masalimo 120-134

  • Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Thandizo Langa Lichokera kwa Yehova”: (10 min.)

    • Sal. 121:1, 2—Popeza Yehova analenga zonse, tiyenera kumamukhulupirira kwambiri (w04 12/15 12 ndime 3)

    • Sal. 121:3, 4—Yehova amakhala tcheru nthawi zonse kuti aone zimene atumiki ake akufunikira (w04 12/15 13 ndime 4)

    • Sal. 121:5-8—Yehova ndi wokhulupirika ndipo amateteza anthu ake (w04 12/15 13 ndime 5-7)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Sal. 123:2—Kodi fanizo la “maso a atumiki,” kapena kuti akapolo, lili ndi mfundo yotani? (w06 9/1 15 ndime 4)

    • Sal. 133:1-3—Kodi mavesi amenewa akutiphunzitsa chiyani? (w06 9/1 16 ndime 3)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Sal. 127:1–129:8

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) wp16.5 tsamba loyamba—Kukambirana ndi mwini nyumba yemwe wakwiya.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) wp16.5 tsamba loyamba—Muitanireni kumisonkhano yathu.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 8 ndime 6—Thandizani wophunzira wanu kuti azigwiritsa ntchito zimene waphunzira.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 114

  • Yehova Wandichitira Zazikulu: (15 min.) Onerani vidiyo ya pa jw.org. Yehova Wandichitira Zazikulu. (Pitani pamene palembedwa kuti ZOKHUDZA IFEYO > ZIMENE TIMACHITA.) Kenako kambiranani mafunso awa: Kodi Yehova anathandiza bwanji Crystal ndipo zimenezi zamulimbikitsa bwanji? Kodi amachita chiyani akayamba kuganizira zinthu zoipa zimene zinamuchitikira? Kodi mwaphunzira chiyani pa zimene zinachitikira Crystal?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 6 ndime 15-23, bokosi patsamba 57 ndi Mfundo Zofunika Kuganizira patsamba 58

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 119 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena