Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsamba 6
  • September 26–October 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 26–October 2
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 September tsamba 6

September 26–October 2

MASALIMO 142-150

  • Nyimbo Na. 134 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova ndi Wamkulu ndi Woyenera Kutamandidwa Kwambiri”: (10 min.)

    • Sal. 145:1-9​—Ukulu wa Yehova ndi wosasanthulika (w04 1/15 10 ndime 3-4; 11 ndime 7-8; 14 ndime 20-21; 15 ndime 2)

    • Sal. 145:10-13​—Atumiki a Yehova okhulupirika amayesetsa kumutamada (w04 1/15 16 ndime 3-6)

    • Sal. 145:14-16​—Yehova amafunitsitsa kuthandiza atumiki ake (w04 1/15 17-18 ndime 10-14)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Sal. 143:8​—Kodi lembali lingatithandize bwanji kuti tizilemekeza Yehova tsiku lililonse? (w10 1/15 21 ndime 1-2)

    • Sal. 150:6​—Kodi lemba lomaliza la m’buku la Masalimo limatsindika mfundo yotani? (w13 11/15 4 ndime 4; it-2-E 448)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Sal. 145:1-21

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) 1 Pet. 5:7​—Kuphunzitsa Choonadi.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Sal. 37:9-11​—Kuphunzitsa Choonadi.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 9 ndime 3​—Thandizani wophunzira wanu kuti azigwiritsa ntchito zimene waphunzira.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 99

  • “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki​—Tizilimbikitsa Anthu Achidwi Kuti Azifika Kumisonkhano Yathu”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Konzani zoti pagawidwe timapepala toitanira anthu kumisonkhano yathu ndipo kenako kambiranani mwachidule tsamba 2. Onetsani vidiyo yosonyeza wofalitsa akuitanira munthu amene amamupatsa magazini kumisonkhano yathu. Pomaliza kambiranani kabokosi kakuti, “Zomwe Tidzagawire mu October: Kapepala Koitanira Anthu Kumisonkhano.”

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 7 ndime 15-27, Mfundo Zofunika Kuziganizira patsamba 66

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 145 ndi Pemphero

    Kumbukirani kuti, muyenera kuika nyimboyi kuti onse aimvetsere kenako muibwerezenso kuti onse aimbe nawo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena