Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 3
  • September 9-15

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 9-15
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 3

September 9-15

AHEBERI 9-10

  • Nyimbo Na. 10 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Chithunzi cha Zinthu Zabwino Zimene Zikubwera”: (10 min.)

    • Aheb. 9:12-14​—Magazi a Khristu ndi apamwamba kwambiri kuposa a mbuzi komanso a ng’ombe (it-1 862 ¶1)

    • Aheb. 9:24-26​—Khristu anakapereka mtengo wa nsembe yake kwa Mulungu ndipo anachita zimenezi kamodzi kokha (cf 183 ¶4)

    • Aheb. 10:1-4​—Chilamulo chinkaimira zinthu zabwino zimene zikubwera m’tsogolo (it-2 602-603)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Aheb. 9:16, 17​—Kodi mavesiwa akutanthauza chiyani? (w92 3/1 31 ¶4-6)

    • Aheb. 10:5-7​—Kodi ndi liti pamene Yesu analankhula mawu amenewa, nanga ankatanthauza chiyani? (it-1 249-250)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Aheb. 9:1-14 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 1)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 2)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako musiyireni khadi lodziwitsa anthu za jw.org. (th phunziro 11)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 89

  • Kodi Timayamikira Misonkhano Yathu? (Sal. 27:11): (12 min.) Onerani vidiyoyi. Kenako kambiranani mafunso otsatirawa:

    • Kodi ndi zinthu ziti zomwe Yesu, yemwe ndi Mkulu wa Ansembe, akutichitira masiku ano?

    • Kodi tingasonyeze kuyamikira m’njira zitatu ziti?

  • Muzimvetsera Pamisonkhano: (3 min.) Onerani vidiyoyi. Kenako pemphani ana kuti afotokoze chifukwa chake ayenera kumamvetsera akakhala pamisonkhano.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 50

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 128 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena