Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 5
  • September 23-29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 23-29
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 5

September 23-29

AHEBERI 12-13

  • Nyimbo Na. 88 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Chilango Chimasonyeza Kuti Yehova Amatikonda”: (10 min.)

    • Aheb. 12:5​—Mukapatsidwa chilango, musamakhumudwe n’kusiya kuchita zoyenera (w12 3/15 29 ¶18)

    • Aheb. 12:6, 7​—Yehova amalanga anthu amene amawakonda (w12 7/1 21 ¶3)

    • Aheb. 12:11​—Ngakhale kuti chilango ndi chowawa, chimatithandiza kuti tikhale anthu abwino (w18.03 32 ¶18)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Aheb. 12:1​—Kodi chitsanzo cha ‘mtambo waukulu wa mboni’ chimatilimbikitsa bwanji? (w11 9/15 17-18 ¶11)

    • Aheb. 13:9​—Kodi vesili limatanthauza chiyani? (w89 12/15 22 ¶10)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Aheb. 12:1-17 (th phunziro 11)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza wachiwiri. (th phunziro 2)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) lvs 39-40 ¶19 (th phunziro 6)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 115

  • Tizikhalabe Okhulupirika . . . Ngakhale Kuti si Ife Angwiro: (5 min.) Onerani vidiyoyi. Kenako kambiranani mafunso otsatirawa:

    • Kodi M’bale Cázares wakhala akulimbana ndi vuto lotani kungochokera pamene anayamba kutumikira Yehova?

    • Kodi m’baleyu anathandizidwa bwanji?

  • Zofunika Pampingo: (10 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 52

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 93 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena