Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 6
  • September 30–October 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 30–October 6
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 6

September 30–October 6

YAKOBO 1-2

  • Nyimbo Na. 122 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kuganizira Zoipa N’koopsa”: (10 min.)

    • [Onerani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Yakobo.]

    • Yak. 1:14​—Kuganizira zolakwika kumachititsa kuti munthu ayambe kulakalaka zoipa (g17.4 14)

    • Yak. 1:15​—Kulakalaka zoipa kungachititse kuti munthu achite tchimo lomwe pamapeto pake limabweretsa imfa (g17.4 14)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yak. 1:17​—N’chifukwa chiyani Yehova amatchedwa “Atate wa zounikira zonse zakuthambo”? (it-2 253-254)

    • Yak. 2:8​—Kodi “lamulo lachifumu” n’chiyani? (it-2 222 ¶4)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yak. 2:10-26 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Wobwereza Wachitatu: (Osapitirira 3 min.) Sankhani lemba lililonse. Muitanireni kumisonkhano yathu. (th phunziro 3)

  • Ulendo Wobwereza Wachitatu: (Osapitirira 4 min.) Sankhani lemba lililonse. M’patseni buku kapena kabuku kamene timagwiritsa ntchito pophunzira ndi anthu. (th phunziro 12)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) bhs 30 ¶4-5 (th phunziro 13)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 45

  • “Pitirizani Kuganizira Zimenezi”: (8 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muzipewa Zinthu Zimene Zingawononge Khalidwe Lanu la Kukhulupirika​—Zosangalatsa Zosayenera.

  • Makolo, Muzithandiza Ana Anu Kudziwa Kuopsa Kotumizirana Zinthu Zolaula: (7 min.) Nkhani yokambidwa ndi mkulu, yochokera mu Galamukani! ya November 2013 tsamba 4-5.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 53

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 142 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena