Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsamba 5
  • January 20-26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • January 20-26
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 January tsamba 5

January 20-26

GENESIS 6-8

  • Nyimbo Na. 89 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Anachitadi Momwemo”: (10 min.)

    • Gen. 6:9, 13​—Nowa anali wolungama koma ankakhala pakati pa anthu oipa (w18.02 4 ¶4)

    • Gen. 6:14-16​—Nowa anapatsidwa ntchito yovuta (w13 4/1 14 ¶1)

    • Gen. 6:22​—Nowa ankakhulupirira Yehova (w11 9/15 18 ¶13)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 7:2​—Kodi zinyama anazisiyanitsa kuti zina ndi zodetsedwa pomwe zina n’zosadetsedwa potengera mfundo yotani? (w04 1/1 29 ¶7)

    • Gen. 7:11​—Kodi madzi amene anachititsa Chigumula padziko lonse anachokera kuti? (w04 1/1 30 ¶1)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 6:1-16 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi ndipo kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi wofalitsa wagwiritsa ntchito bwanji lemba la 1 Yohane 4:8, pokambirana ndi mwininyumba? Kodi ofalitsawa anathandizana bwanji pomulalikira munthuyu?

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 4 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 12)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. Kenako mugawireni chilichonse cha zinthu zomwe timagwiritsa ntchito pophunzitsa. (th phunziro 7)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 31

  • Kulambira kwa Pabanja​—Nowa Anayenda ndi Mulungu: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako kambiranani mafunso otsatirawa: Kodi m’vidiyoyi, makolo anagwiritsa ntchito bwanji nkhani ya m’Baibulo ya Nowa pophunzitsa ana awo? Kodi ndi mfundo zabwino ziti zomwe mungazigwiritse ntchito pa kulambira kwanu kwa pa banja?

  • Zofunika Pampingo: (5 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 69

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 40 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena