Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsamba 2
  • February 3-9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • February 3-9
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 February tsamba 2

February 3-9

GENESIS 12-14

  • Nyimbo Na. 14 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Pangano Lomwe Limakukhudzani”: (10 min.)

    • Gen. 12:1, 2​—Yehova analonjeza kuti adzadalitsa Abulamu (Abulahamu) (it-1 522 ¶4)

    • Gen. 12:3​—“Mabanja onse a padziko lapansi adzapeza madalitso chifukwa cha [Abulahamu]” (w89 7/1 3 ¶4)

    • Gen. 13:14-17​—Yehova anaonetsa Abulahamu dziko limene anadzalipereka kwa ana ake (it-2 213 ¶3)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 13:8, 9​—Kodi tingatsanzire bwanji Abulahamu pa nkhani yopewa mikangano? (w16.05 5 ¶12)

    • Gen. 14:18-20​—Kodi Levi “anapereka zakhumi” kudzera mwa Abulahamu m’njira yotani? (Ahe 7:4-10; it-2 683 ¶1)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 12:1-20 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Kuthandiza Anthu Kuti Aone Mfundo Zazikulu, kenako kambiranani phunziro 14 m’kabuku ka Kuphunzitsa.

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) w12 1/1 8​—Mutu: N’chifukwa Chiyani Tinganene Kuti Sara Anali Mkazi Wabwino Kwambiri? (th phunziro 14)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na 144

  • “Kodi Tingaphunzire Chiyani Kuchokera mu Nyimbo za Broadcasting?”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yanyimbo yakuti Dziko Latsopano Lili Pafupi.

  • Zofunika Pampingo: (5 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 71

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 34 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena