Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsamba 4
  • June 15-21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 15-21
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 June tsamba 4

June 15-21

GENESIS 48-50

  • Nyimbo Na. 30 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Achikulire Angatiphunzitse Zambiri”: (10 min.)

    • Gen. 48:21, 22​—Yakobo anali ndi chikhulupiriro kuti Aisiraeli adzalanda dziko la Kanani (it-1 1246 ¶8)

    • Gen. 49:1​—Ulosi umene Yakobo analosera atatsala pang’ono kufa unasonyeza kuti anali ndi chikhulupiriro (it-2 206 ¶1)

    • Gen. 50:24, 25​—Yosefe anali ndi chikhulupiriro kuti Yehova adzakwaniritsa zimene analonjeza (w07 6/1 28 ¶10)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 49:19​—Kodi zimene Yakobo analosera zokhudza Gadi zinakwaniritsidwa bwanji? (w04 6/1 15 ¶4-5)

    • Gen. 49:27​—Kodi zimene Yakobo analosera zokhudza Benjamini zinakwaniritsidwa bwanji? (it-1 289 ¶2)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 49:8-26 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi ofalitsawa anachitira bwanji zinthu limodzi mogwirizana polalikira? Kodi tingatsanzire bwanji ofalitsawa posonyeza kuti timakhulupirira zimene tikunena tikakhala mu utumiki?

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 6)

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako mugawireni buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa ndipo yambitsani phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito mutu 9 (th phunziro 16)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 138

  • “Zimene Tingaphunzire kwa Akhristu Omwe Atumikira kwa Nthawi Yaitali”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Kukhalabe Ogwirizana Panthawi Imene Ntchito Yathu Inali Yoletsedwa.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 88 ndime 1-11

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 61 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena