Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsamba 8
  • August 31–September 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 31–September 6
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 August tsamba 8

August 31–September 6

EKISODO 21-22

  • Nyimbo Na. 141 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Muzisonyeza Kuti Mumaona Moyo Mmene Yehova Amauonera”: (10 min.)

    • Eks 21:20​—Yehova amaletsa kupha munthu (it-1 271)

    • Eks 21:22, 23​—Yehova amaona kuti moyo wa mwana amene sanabadwe ndi wamtengo wapatali (lvs 95 ¶16)

    • Eks 21:28, 29​—Yehova amafuna kuti tizichita zinthu mosamala kuti tizipewa ngozi (w10 4/15 29 ¶4)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 21:5, 6​—Kodi mavesiwa akusonyeza bwanji kuti kudzipereka kwa Yehova n’kothandiza? (w10 1/15 4 ¶4-5)

    • Eks 21:14​—Kodi vesili tingalifotokoze bwanji? (it-1 1143)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 21:1-21 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako muitanireni kumisonkhano yathu. (th phunziro 2)

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako musonyezeni ndi kukambirana naye mfundo za m’vidiyo yakuti Kodi pa Nyumba ya Ufumu Pamachitika Zotani? (koma musaonetse vidiyoyi). (th phunziro 20)

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) w09 4/1 31​—Mutu: Yehova Ndi Atate wa Ana Amasiye. (th phunziro 19)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 60

  • Muziona Moyo Mmene Yehova Amauonera: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani mafunso awa: Ndi mavuto otani amene mayi angakumane nawo akakhala woyembekezera? Mogwirizana ndi Ekisodo 21:22, 23, kodi nkhani yochotsa mimba timaiona bwanji? N’chifukwa chiyani chikhulupiriro komanso kulimba mtima n’zofunika kuti tisankhe kuchita zinthu zosangalatsa Yehova? Kodi chiyembekezo chakuti akufa adzauka chimatilimbikitsa bwanji?

  • Mmene Kudzipereka Kumatithandizira: (5 min.) Nkhani yochokera mu Nsanja ya Olonda ya January 15, 2010, tsamba 4, ndime 4-7. Limbikitsani ophunzira Baibulo kuti afike podzipereka kwa Yehova komanso kubatizidwa.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 98

  • Mawu Omaliza (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 18 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena