Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 May tsamba 14
  • June 21-27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 21-27
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 May tsamba 14

June 21-27

DEUTERONOMO 7-8

  • Nyimbo Na. 136 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Usadzachite Nawo Mgwirizano wa Ukwati”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • De 8:3​—Kodi tingaphunzire chiyani pa mana amene Yehova ankapatsa Aisiraeli? (w04 2/1 13 ¶4)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) De 7:1-16 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Muitanireni kumisonkhano yathu. (th phunziro 15)

  • Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 9)

  • Nkhani: (5 min.) w06 1/1 28 ¶14-15​—Mutu: Musaiwale Yehova. (th phunziro 7)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 35

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (5 min.) Onerani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya June.

  • Zofunika Pampingo: (10 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 139 ndi bokosi lakuti “Kuti Mutsanzire Yesu Muyenera . . . ”

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 139 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena