Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 November tsamba 6
  • November 22-28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • November 22-28
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 November tsamba 6

November 22-28

OWERUZA 1-3

  • Nyimbo Na. 126 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Nkhani ya Kulimba Mtima Komanso Yochititsa Chidwi”: (10 min.)

    Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Owe 2:10-12​—Kodi nkhani imeneyi ikutichenjeza chiyani ifeyo? (w05 1/15 24 ¶7)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Owe 3:12-31 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • “Zimene Mungachite Kuti Muzisangalala Kwambiri mu Utumiki​—Muzilola Kuti Yehova Azikuthandizani Kudzera M’pemphero”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muzigwiritsa Ntchito Zomwe Yehova Watipatsa Kuti Muzisangalala ndi Ntchito Yophunzitsa​—Pemphero.

  • Phunziro la Baibulo: (5 min.) lffi phunziro 02 mawu oyamba komanso mfundo 1-3 (th phunziro 11)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 53

  • Khalani Bwenzi la Yehova​—Uzichita Zinthu Bwino mu Utumiki: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako ngati n’kotheka, pemphani ana amene munawasankhiratu kuti abwere kupulatifomu ndipo afunseni mafunso awa: Kodi tingakonzekere bwanji utumiki? Kodi tingatani kuti tizioneka bwino komanso tizivala mwaulemu? Kodi tingatani kuti tizisonyeza makhalidwe abwino mu utumiki?

  • “Mfundo Zothandiza Kuti Msonkhano Wokonzekera Utumiki Uzikhala Wabwino”: (10 min.) Nkhani yokambirana yokambidwa ndi woyang’anira utumiki. Funsani omvera kuti afotokoze ubwino wofika pa msonkhano wokonzekera utumiki mwamsanga.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs mutu 8 ndime 1-7

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 31 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena