Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 January tsamba 8
  • January 30–February 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • January 30–February 5
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 January tsamba 8

January 30–February 5

1 MBIRI 7-9

  • Nyimbo Na. 84 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Angakuthandizeni Kuti Mukwanitse Kuchita Utumiki Wovuta”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • 1Mb 9:33​—Kodi vesili likutithandiza bwanji kumvetsa kuti nyimbo ndi zofunika kwambiri pa kulambira koona? (w10 12/15 21 ¶6)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) 1Mb 7:1-13 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Mugawireni khadi lodziwitsa anthu za jw.org. (th phunziro 16)

  • Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 20)

  • Nkhani: (5 min.) w21.06 3-4 ¶3-8​—Mutu: Muzithandiza Wophunzira Baibulo Kuti Azigwiritsa Ntchito Zimene Akuphunzira. (th phunziro 13)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 38

  • “Yehova Amatithandiza Tikamakumana ndi Mayesero”: (15 min.) Nkhani yokambirana komanso vidiyo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 36

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 31 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena