Magazini Yophunzira
March 2020
NKHANI ZOPHUNZIRA: MAY 4-31, 2020
© 2019 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo. Ngati mukufuna kupereka pitani pa donate.jw.org.
Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.
CHITHUNZI CHAPACHIKUTO:
Usiku woti aphedwa mawa lake, Yesu anatsindika mfundo ya chikondi kwa ophunzira ake (Onani nkhani yophunzira 13, ndime 1-2)