Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwfq nkhani 6
  • Kodi a Mboni za Yehova Amakhulupirira Yesu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi a Mboni za Yehova Amakhulupirira Yesu?
  • Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
  • Nkhani Yofanana
  • Yesu Kristu—Kodi Anatumidwa ndi Mulungu?
    Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • Kodi Mboni za Yehova Zimakhulupirira Chiyani?
    Kodi Mboni za Yehova Zimakhulupirira Chiyani?
  • “Njira Choonadi ndi Moyo”
    ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’
  • Yesu Kristu, kupyolera mwa Amene Mulungu Adzawadalitsa Anthu
    Coonadi Cimene Cimatsogolera ku Moyo Wamuyaya
Onani Zambiri
Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
ijwfq nkhani 6
Yesu akufa

Kodi a Mboni za Yehova Amakhulupirira Yesu?

Inde. Timakhulupirira Yesu amene anati: “Ine ndine njira, choonadi ndi moyo. Palibe amene amafika kwa Atate osadzera mwa ine.” (Yohane 14:6) Timakhulupirira kuti Yesu anabwera padziko lapansi kudzapereka moyo wake wangwiro monga nsembe yowombola anthu. (Mateyu 20:28) Chifukwa chakuti iye anafa komanso kuukitsidwa, zimakhala zotheka kuti anthu amene amamukhulupirira adzapeze moyo wosatha. (Yohane 3:16) Timakhulupiriranso kuti panopa Yesu akulamulira monga Mfumu mu Ufumu wakumwa wa Mulungu, umene posachedwapa udzabweretsa mtendere padziko lonse lapansi. (Chivumbulutso 11:15) Komabe, timaona Yesu mogwirizana ndi zimene iyeyo ananena pamene anati: “Atate ndi wamkulu kuposa ine.” (Yohane 14:28) Choncho sitilambira Yesu popeza timadziwa kuti iyeyo si Mulungu Wamphamvuyonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena